

Mary Chilima wayamikila Mutharika mtsogoleri wa Malawi pofufuza imfa ya Chilima
Mayi Mary Chilima mkazi wa yemwe anali wachiwiri kwa President wa dzikolo Dr Saulos Klaus Chilima wayamikila ganizo la mtsogoleri wa dzikolo Professor Arthur Peter Mutharika lokuti pakhalenso kafufuku wina wa ngozi ya ndege yomwe inapha a Chilima ndi anthu ena asanu ndi atatu (8) m' mwezi wa June m…

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
Kachilombo ka matenda a Polio type 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka mdziko la Zambia ndipo kachilomboka kakufanana ndi kachilombo kamene kanapezeka m’mayiko a Namibia ndi Angola. Ziyenela Zimba wabwela ndi nkhani yonse

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
President wa dziko la Zambia Hakainde Hichilema wachotsa ntchito nduna ya za umoyo, a Elijah Muchima ndi nduna ya ntchito za malonda zing'ono-zing'ono, a Elias Mubanga ndipo mkulu yemwe amafalitsa nkhani zaku nyumba ya boma ya President, Clayson Hamasaka, ndi amene walengeza nkhaniyi mu chikalata c…

Zipani zina zotsutsa boma ku Zambia sizikufuna kuwonjezela aphungu 70
Zipani zingapo zotsutsa boma mdziko la Zambia kuphatikizapo chipani cha Forum for Democracy and Development, FDD, ndi mabungwe ena wodziyimira pa okha, akana kutengako mbali ku zokambilana zakuchulukitsa chiwerengero cha aphungu ndi 70. Bungwe lomwe limayendetsa zisankho mdzikolo la Electoral Comm…

Anthu ambiri Ku Malawi akufuna pakhale lamulo loti opha nzake aziphedwa
Anthu ambiri akufuna kuti boma likhazikitse lamulo loti opha nzake naye aziphedwa, ndikuti president azisainira. Izi zadza pamene mchitidwe ophana chisawawa ukunka nuchulukira ku Malawi. Sabata yatha ku Mwanza anthu anapeza mafupa a ana aakazi awiri wina zaka 10 wina 12 mminda yosiyana, atasowa k…

Anthu ambiri Ku Malawi akufuna pakhale lamulo loti opha nzake aziphedwa
Anthu ambiri akufuna kuti boma likhazikitse lamulo loti opha nzake naye aziphedwa, ndikuti president azisainira.Izi zadza pamene mchitidwe ophana chisawawa ukunka nuchulukira ku Malawi. Sabata yatha ku Mwanza anthu anapeza mafupa a ana aakazi awiri wina zaka 10 wina 12 mminda yosiyana, atasowa kw…

Anthu 17 000 alibe magetsi ku Mozambique kamba ka Namondwe wa Gezani
Anthu a ku m’mwela kwa dziko la Mozambique maka maka mchigawo cha Inhambane, akhuzidwa kwambili ndi namondwe wa Gezani pamene anthu oposela 17,000 alibe magetsi komanso mabanja 880 akusowelatu pokhala. Bright Sonjela akufotokoza Zambiri

Boma la Malawi lakana kubweleka ndalama zochuluka kwa makampani
Boma la dziko la Malawi lakana kubweleka ndalama zochuluka kwa ochita malonda ndi makampani a mdzikolo chifukwa likufuna kubweza ngongole zomwe lili nazo kale . George Mhango akusimba

Mphekesela ikuti Bungwe la masankho ku Zambia la ECZ likufuna kusintha malamulo
Pakumveka manong'onong'o akuti bungwe lomwe limayendetsa zisankho mdziko la Zambia la Electoral Commission of Zambia, ECZ, likufuna kusintha mfundo zina za malamulo oyendetsera zisankho. Nkhaniyi yabweretsa mantha pakati pa zipani zotsutsa boma. Poyamba Daniel Elisha Banda walankhulana ndi mkulu …

Alimi ku Malawi ayambanso kugulitsa chimanga ku NFRA
Boma la Malawi kudzela mu bungwe lowona za chakudya la National Food Reserve Agency NFRA, layambanso kugula chimanga kwa alimi pamene linasiya kugula chimanga masiku apitawo chifukwa chokuti ndalama zogulira zinatha. George Mhango wabwela ndi nkhani yonse .