

Tonse Alliance ku Zambia yawina masankho a dela Chawama
Zipani za mgwirizano zotsutsa boma za mdziko la Zambia za Tonse Alliance zapambana chisankho cha phungu ku dera la Chawama mu mzinda wa Lusaka. Masankhowa achitika dzulo pambuyo pa yemwe kale anali phungu wa deralo, Tasila Lungu, kuchotsedwa pa mpando ndi nyumba ya malamulo . Ichi ndi chifukwa ch…

Anthu a chi alubino akupitilira kuchitidwa nkhanza ku Malawi
Mchitidwe ochitila nkhanza anthu a chi Alubino wayambilanso m’madela ena a mdziko la Malawi ndipo mtsogoleri wa bungwe la APAM la anthu a chi alubino Young Muhamba, wati akufuna kuti akadandaule za mchitidwewu kwa mtsogoleri wa dzikolo Professor Arthur Peter Mutharika. Jayne Chilimampunga akutamba…

Alimi ena ku Zambia akudikilabe boma liwapatse malipiro atagulitsa mbewu ku FRA
Alimi ambiri mdziko la Zambia, akudandaula kuti boma likuchedwa kuwapatsa ndalama zawo pa zokolola zawo zomwe anagulitsa ku bungwe la boma lowona za chakudya la Food Reserve agency chaka chatha pamene boma linalonjeza kuti liwalipira alimi onse a mdzikolo pofika pa 10 January chaka chino. Ziyenela…

Akatswili a ndale ati A Mutharika akutsogolera bwino Malawi
Akatswili osiyana siyana a mdziko la Malawi, alankhulapo pa za mtsogoleri wa dzikolo professor Arthur Peter Mutharika, kukwanitsa masiku 100 chiyambileni kulamula pambuyo popambana masankho chaka chatha. George Mhango akusimba.

MICHAEL CHANG AKUFUNA KUTI ATULUTSIDWE MNDENDE KU AMERICA
Yemwe kale anali Nduna ya za chuma mdziko la Mozambique Manuel Chang, wapita ku bwalo la Federal mdziko la USA pa kufuna kuti limve pempho lake lofuna kuti atulutsidwe mndende. Bright Sonjera akufotokoza

OPHUNZIRA AYAMBA KUPHUNZIRA MWA ULERE MDZIKO LA MALAWI
Pamene ophunzira ayamba kuphunzira mwa ulere mdziko la Malawi,akatswiri pa nkhani za ndale komanso maphunziro ayankhulapo pa kufunika kwa bvoma kuonjezera malo ogonera pa masukulu ena a maphunziro. Jane Chilimampunga

KULANDIRA MSONKHO MU NDALAMA YA DZIKO LA CHINA KU ZAMBIA
Nduna ya za chuma mdziko la Zambia Situmbeko Musotokwane, yalengeza kuti boma tsapano lidzilola Ochita malonda a za migodi kuti adzipereka misonkho kugwiritsira ndalama ya dziko la China kuphatikiza ya dziko America. Ziyenela Zimba akufotokoza zambiri

PRESIDENTI WA DZIKO LA MALAWI WASINTHA NDUNA ZAKE
Presidenti wa dziko la Malawi, Professor Arthur Peter Mutharika, wasintha nduna zake za boma patangodutsa miyezi itatu iye kukhala mtsogoleri wa dzikolo. Mtolankhani wa Channel Africa George Mhango wafotokoza zambiri.

NGOZI ZA PA NSEWU ZIKUKUPITILIRA KUKWERA KU MALAWI
Ngozi za pa nsewu zikupitilira kukwera mdziko la Malawi, ndipo pali mafunso pa zomwe zikupangitsa izi. Anthu ambiri akutaya miyoyo yawo ndipo ena akubvulala modetsa nkhawa. Mtolankhani wa Channel Africa Jane Chilimampunga, walankhula ndi katswiri pa nkhani zosiyana siyana mdzikolo Bernard Mwanza, y…

Aphungu achipani cha PF ku Zambia omwe anavotela bill 7 akuwopsyezedwa
Pali manong’o-non’go akuti aphungu achipani chotsutsa boma cha Patriotic Front, PF, mdziko la Zambia amene anavotela Bill 7 akumaopsyezedwa ndi anthu osadziwika bwino kuti adzaphedwa. M’modzi mwa akuluakulu achipanichi, Philip Bobat Phiri wati nkhani ya ziopsyezo ndi yoipa komabe aphungu achipani c…