Mayi Mary Chilima mkazi wa yemwe anali wachiwiri kwa President wa dzikolo Dr Saulos Klaus Chilima wayamikila ganizo la mtsogoleri wa dzikolo Professor Arthur Peter Mutharika lokuti pakhalenso kafufuku wina wa ngozi ya ndege yomwe inapha a Chilima ndi anthu ena asanu ndi atatu (8) m' mwezi wa June mchaka cha 2024. George wabwera ndi tsatane tsatane wa nkhaniyi

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
05:48

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
08:43

Zipani zina zotsutsa boma ku Zambia sizikufuna kuwonjezela aphungu 70
08:17