



Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
Sipikala wa nyumba ya malamulo ya mdziko la Malawi Sameer Suleman wakhazikitsa committee yatsopano yapadela yomwe ichite yakafuku fuku wa ngozi yomwe inapha wachiwiri kwa president Dr Saulos Chilima ndi anthu ena asanu ndi atatu ndipo ku committee imeneyi mukhala aphungu oyima pa okha ndi aphun…

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
Mtsogoleri wachipani chotsutsa boma cha National Unity Platform NUP ku Uganda a Robert Chagulanyi Sentamu omwe amadziwikanso kuti Bobi Wine atuluka m'dziko la Uganda. Zifukwa zeni zeni zomwe iwo atulukira mdzikolo sizikudziwika koma a Bobi Wine akhala akunena kuti moyo wawo unali pa chiopsyezo ndi…

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
Zigao zonse khumi za dziko la Zambia lero zachita chisangalalo cha achinyamata cha Youth Day ndipo chapmutu cha chaka chino chili motere: Dzukani ndi Kuuluka . Koma chisangalalo chachikulu cha dziko lonse chayendetsedwa ndi President Hakainde Hichilema mu boma la Solwezi ku chigao cha North-wester…

Mchitidwe wa uchifwamba ukuchulukila ku Malawi
Pambuyo pakubedwa kwa mwini wa crossroads hotel ku Lilongwe mdziko la Malawi, tsopano anthu ayamba kumasowa, ena kubedwa kumene, pomwenso ena akumapezeka ataphedwa patapita masiku. Ena akumawaba nkukawagwi-li-li-ra atawamwetsa mankhwala ogonetsa. Jayne Chilimampunga wabwela ndi nkhani yonse.

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wati amayi ndi ofunikila kwambiri
Mtsogoleri wa dziko la Zambia Hakainde Hichilema, wafotokoza kuti azimai ndi nsanamira zofunikira kwambiri pa zitukuko za dziko. A Hichilema analankhula mauwa dzulo pa mwambo wokumbukira tsiku la amai pa dziko lonse lapansi limene cha pamutu chake chinali motere: Danga, Chilungamo, Kuchitapo Kanth…

Mpungwe pungwe wabuka mchipani chotsutsa boma ku Malawi cha MCP
Mpungwepungwe wabuka mchipani chotsutsa boma cha Malawi Congress Party--MCP mdziko la Malawi pomwe kagulu kena kakufuna mtsogoleri wa Chipanichi Dr Lazarus Chakwera kuti atule pansi udindo wawo pomwe ena akuti kaguluko kangotumidwa chabe. Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka a…

A Malawi ambiri apempha ACB kuti ifufuze katangale ku polisi
Anthu ambiri mdziko la Malawi apempha bungwe lothana ndi katangale la ACB kuti afufuze za mchitidwe wa katangale ku nthambi ya polisi pamene apolisi akumapempha ndalama kwa anthu kuti achite ntchito yawo.Jayne Chilimampunga wabwela ndi nkhani yonse

Boma la Zambia latolera K53 biliyoni ku ntchito zosiyana siyana
Boma la Zambia lapeza ndalama zambiri ku ntchito zosiyana siyana kuphatikiza malonda komanso kuchokela ku thandizo la mabungwe akunja zokwana 53 billion kwacha ya dzikolo mchaka cha 2025. Ziyenela Zimba akufotokoza zambiri

Boma la Zimbabwe layimitsa kugulitsa miyila ya mtengo wapatali kunja
Boma la Zimbabwe lalengeza kuti kugulitsa miyala ya mtengo wa patali kuyimitsidwe kufikila mtsogolo chifukwa chokuti miyala imagulitsidwa osasulidwa zomwe zimapangitsa kuti miyala izigulitsidwa motsika mtengo. John Kassim akulongosola

Bungwe la MERA ku Malawi lakweza gasi ndi 19.65%
Bungwe lowona za mafuta mdziko la Malawi la Malawi Energy Regulatory Authority MERA, lakweza mtengo wa gasi ndi 19.65 pelecenti kuchoka pa K3,740 kufika pa K4,475.00 pa kilogram imodzi ndipo bungweli lati mafuta a galimoto a Petrol ndi diesel saakwera mtengo. George Mhango akufotokoza zambiri.