



Venancio Mondlane wati anthu alile maliro a Anselmo Vicente ku Mozambique
Mtsogoleri wa chipani chosutsa boma mdziko la Mozambique cha Anamola Venancio Mondlane, wapempha kuti pakhale masiku atatu olira maliro a m’modzi mwa akulu akulu a chipanichi Anselmo Vicente amene anaphedwa loweluka lapitali mtawuni ya Chimoio mchigawo cha Manica. Bright Sonjela akufotokoza tsata…

AIPAC ku Zambia yatsuta kuwunika ma bilu pomwe paliyamenti itseke pa 15 May 2026
Bungwe lodziyimira palokha m’dziko la Zambia la Action for Policy Analysis Centre, AIPAC, ladzudzula nyumba ya malamulo chifukwa chofuna kuwunika ma bilu oposa 70 pomwe kwatsala masiku atatu okha kuti itsekedwe. Mkulu wa bungweli, Solomon Ngoma, akuti ntchito yopanga malamulo ndi yofunika koma ikuc…

Anthu 7 aphedwa ku Malawi pogawaganizila kuti akusowetsa maliseche
Anthu asanu ndi awiri (7)aphedwa masiku apitawa m’maboma a Chikwawa ndi Nsanje mdziko la Malawi powaganizila kuti anasowetsa maliseche a anthu ena. Jayne Chilimampunga ali ndi nkhaniyi

Bungwe la CHREA ku Malawi likufuna kuti akaidi azichita za dama ndi akazi awo
Pali maganizo osiyana mdziko la Malawi pa za ufulu wa akaidi oti azipatsidwa mpata okhala malo amodzi ndi okondedwa awo pa nthawi yomwe akuphika ndende mdziko la Malawi. Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.

Boma la Mozambique lamanga akulu akulu omwe amaba ndalama za penshoni
Boma la Mozambique lamanga akulu akulu omwe amaba ndalama za nthambi ya pension ya ENSS. Bright Sonjela akufotokoza.

Mtsogoleri wa Malawi Arthur Mutharika wakana mphekesela yokuti akudwala
President wa dziko la Malawi Professor Arthur Peter Mutharika, watsutsa mphekesera zokuti akudwala mwakaya-kaya ndipo wapititsidwa ku Chipitala mdziko la South Africa.Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka wadza ndi zambiri.

Dziko la Zambia lakondwelera mtsogoleri oyamba Kenneth Kaunda
Mu mzinda wa Lusaka, nzika za Zambia lero zinasonkhana kukumbukira tsiku lobadwa komanso mbiri ya mtsogoleri oyamba wa dzikolo Kenneth Kaunda. Atsogoleri a boma, andale, atsogoleri a mipingo komanso akazembe a mayiko osiyanasiyana anasonkhana ku kachisi wa Cathedral of the Holy Cross komwe kwachi…

Alimi ku Zambia azigulitsa fodya pakati 40centi ndi 5 US dollars pa kilo imodzi
Makampani ambiri ogula mbewu ya fodya mdziko la Zambia alengeza mitengo ya chigawo cha ulimi wa 2025/2026. Mitengo ya chaka chino ili pakati pa 40 cents ndi 5 dollars-20 cents pa kg imodzi ndalama ya dziko la America . Daniel Elisha Banda ali ndi nkhani yonse.

Osangalatsa anthu pa masamba a mchezo ku Malawi akumana ndi akulu a Meta
Akulu akulu a meta amchigawo cha ku m’mwela, kwa Africa ali mdziko la Malawi komwe akukumana ndi anthu ochita za msangalutso kapena kuti content creators pa masamba a mchezo komwe akambilane zokuti anthuwa azilipidwa ndalama ndi kampani ya Meta pa zomwe amaponya pa masamba a mchezo. Jayne Chilima…

Anthu opezeka ndi mlandu ogwilira samapatsidwa belo ku Zambia
Boma la Zambia lakhazikitsa lamulo latsopano lomwe likuchotsa belo kwa anthu opalamula milandu yogwilira amai, atsikana komanso kuchita za chiwele wele pa chibale. Lamuloli lidzayamba kugwira ntchito mwezi uno wa April, ndipo likuyembekezeka kuthandiza kuchepetsa nkhanza zogwilira mdzikolo. Daniel …