Pakumveka manong'onong'o akuti bungwe lomwe limayendetsa zisankho mdziko la Zambia la Electoral Commission of Zambia, ECZ, likufuna kusintha mfundo zina za malamulo oyendetsera zisankho. Nkhaniyi yabweretsa mantha pakati pa zipani zotsutsa boma. Poyamba Daniel Elisha Banda walankhulana ndi mkulu wa bungwe la Anti-Voter Apathy Project, AVAP, wa chigao cha Eastern Province, a Maumba Ngoma.

Mary Chilima wayamikila Mutharika mtsogoleri wa Malawi pofufuza imfa ya Chilima
08:31

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
05:48

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
08:43