Boma la Malawi kudzela mu bungwe lowona za chakudya la National Food Reserve Agency NFRA, layambanso kugula chimanga kwa alimi pamene linasiya kugula chimanga masiku apitawo chifukwa chokuti ndalama zogulira zinatha. George Mhango wabwela ndi nkhani yonse .

Mary Chilima wayamikila Mutharika mtsogoleri wa Malawi pofufuza imfa ya Chilima
08:31

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
05:48

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
08:43