Zipani zingapo zotsutsa boma mdziko la Zambia kuphatikizapo chipani cha Forum for Democracy and Development, FDD, ndi mabungwe ena wodziyimira pa okha, akana kutengako mbali ku zokambilana zakuchulukitsa chiwerengero cha aphungu ndi 70. Bungwe lomwe limayendetsa zisankho mdzikolo la Electoral Commission of Zambia, ECZ, layambitsa ntchito yakufunsila maganizo ya mafumu, atsogoleri aza ndale, amipingo ndi ena Lolemba pa 16 February 2026. Daniel Elisha Banda akusimba.

Mary Chilima wayamikila Mutharika mtsogoleri wa Malawi pofufuza imfa ya Chilima
08:31

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
05:48

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
08:43