Wachiwiri kwa a pulezident wa dziko la Kenya a Rigathi Gachagua amuchotsa pa udindo. Izi zikutsatira pomwe aphungu anavoterabe kuti a Gachagua atule pansi udindo wawo kamba ka milandu khumi ndi umodzi, 11 yomwe amawazenga. Mtolankhani nzathu kum’mawa kwa Africa, Alfred Dzaoneni ali ndi zambiri.