President wa dziko la Malawi Lazarus Chakwera wati dzikolo lili ndi miyala yamtengo wapatali yambiri yomwe ingathandizire kukweza chuma cha dzikolo, ngati maiko ena angagule miyalayo.
Izitu zadziwika lero pamwamba pa msonkhano wa mining investment forum omwe ukuchitikira munzinda wa Lilongwe mdzikolo.
Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.