Bungwe la Independent Broadcasting Authority la dziko la Zambia la IBA, latulutsa malamulo atsopano okhudza momwe mawayilesi ndi ma TV ayenera kufalitsira nkhani za chisankho cha dzikolo cha mchaka cha 2026. Mkulu wa bungweli, Webster Malido, wafotokoza kuti malamulowa akhazikitsidwa pofuna kulimbikitsa chilungamo, kusakondera komanso kuteteza mtendere pa nthawi ya kampeni ndi chisankho . Tili ndi zambiri mu lipoti la Daniel Elisha Banda.

Anthu ena ozapisikana pa masankho ku Zambia ali ndi masatifiketi abodza
09:02

Fakitole yopanga feteleza ku Malawi ya a Dzombe ikupita kumapeto
07:38

Atsikana achichepele ambiri akumazipeleka kwa azibambo ku Malawi
06:52