Bungwe la Examinations Council of Zambia, ECZ, lati lapeza ma certificate 10 abodza a Grade 12 kuchokera kwa anthu ena amene akufuna kudzapikisana pa zisankho za pa 13 August 2026. Nkhaniyi yabweretsa nkhawa pakati pa nzika pamene malamulo a dziko la Zambia amafuna kuti munthu aliyense amene akufuna kutenga nawo mbali pa zisankho akhale ndi satifiketi ya Grade 12 ngati chimodzi mwa ziyenerezo zofunikira. Daniel Elisha Banda akutambasula nkhaniyi.

Fakitole yopanga feteleza ku Malawi ya a Dzombe ikupita kumapeto
07:38

Atsikana achichepele ambiri akumazipeleka kwa azibambo ku Malawi
06:52

Bungwe la IBA ku Zambia latulutsa malamulo a kufalitsa nkhani za masankho
08:29