Zochitika (Chinyanja)Zochitika (Chinyanja)

Apolisi ku Kenya amanga nduna yakale chifukwa chonamizila kubedwa

View descriptionShare

Raphael Tuju, yemwe ndi Nduna yakale yoona za ubale pakati pa dziko la Kenya ndi mayiko ena , amupeza ndipo amumanga kamba konamilizira kuti wasowa komanso kuti  anabedwa.Mkulu wotsogolera kafukufuku ku polisi ya Nairobi a Mohamed Amin, anena pa msonkhano wa atolankhani kuti a Tuju anali mkati mwa nyumba yake nthawi yonseyi, ndipo anafotokoza kuti kusowa kwa Tuju kunali  kokonzedwa mwadala osati kubedwa ndi anthu achipongwe. Mtolankhani mzathu ku m'mawa kwa Africa Alfred Dzaoneni ali ndi zambiri.

  • Facebook
  • X (Twitter)
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

In 1 playlist(s)

Zochitika (Chinyanja)

Current Affairs featuring various segments. 
Recent clips
Browse 960 clip(s)