Sipikala wa nyumba ya malamulo ya mdziko la Malawi Sameer Suleman wakhazikitsa committee yatsopano yapadela yomwe ichite yakafuku fuku wa ngozi yomwe inapha wachiwiri kwa president Dr Saulos
Chilima ndi anthu ena asanu ndi atatu ndipo ku committee imeneyi mukhala aphungu oyima pa okha ndi aphungu a zipani za DPP, MCP, UTM ndi UDF . Mtolankhani wa Channel Africa Jayne Chilimampunga wabwela ndi nkhani yonse

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

A katswili andale ena ku Malawi ati a Chakwera sanalankhule bwino pa maliro
06:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50