Mchitidwe ochitila nkhanza anthu a chi Alubino wayambilanso m’madela ena a mdziko la Malawi ndipo mtsogoleri wa bungwe la APAM la anthu a chi alubino Young Muhamba, wati akufuna kuti akadandaule za mchitidwewu kwa mtsogoleri wa dzikolo Professor Arthur Peter Mutharika. Jayne Chilimampunga akutambasula bwino nkhaniyi.

Alimi ena ku Zambia akudikilabe boma liwapatse malipiro atagulitsa mbewu ku FRA
07:55

Akatswili a ndale ati A Mutharika akutsogolera bwino Malawi
06:24

MICHAEL CHANG AKUFUNA KUTI ATULUTSIDWE MNDENDE KU AMERICA
08:31