Anthu asanu ndi awiri (7)aphedwa masiku apitawa m’maboma a Chikwawa ndi Nsanje mdziko la Malawi powaganizila kuti anasowetsa maliseche a anthu ena. Jayne Chilimampunga ali ndi nkhaniyi

Venancio Mondlane wati anthu alile maliro a Anselmo Vicente ku Mozambique
05:46

AIPAC ku Zambia yatsuta kuwunika ma bilu pomwe paliyamenti itseke pa 15 May 2026
10:17

Bungwe la CHREA ku Malawi likufuna kuti akaidi azichita za dama ndi akazi awo
07:53