Zochitika (Chinyanja)Zochitika (Chinyanja)

AIPAC ku Zambia yatsuta kuwunika ma bilu pomwe paliyamenti itseke pa 15 May 2026

View descriptionShare
 

Bungwe lodziyimira palokha m’dziko la Zambia la Action for Policy Analysis Centre, AIPAC, ladzudzula nyumba ya malamulo chifukwa chofuna kuwunika ma bilu oposa 70 pomwe kwatsala masiku atatu okha kuti itsekedwe. Mkulu wa bungweli, Solomon Ngoma, akuti ntchito yopanga malamulo ndi yofunika koma ikuchitika pa nthawi yosayenera chifukwa aphungu ambiri sakumapezeka pa zokambirana zofunika. Daniel Elisha Banda akutambasula nkhaniyi.

  • Facebook
  • X (Twitter)
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

In 1 playlist(s)

Zochitika (Chinyanja)

Current Affairs featuring various segments. 
Recent clips
Browse 975 clip(s)