Ku misonkhano ina ya ndale yokopa anthu mdziko la Malawi kukuchitika zipolowe pamene zipani zayamba kuchita kampeni pokonzekela masankho omwe adzachitike chaka cha mmawa mdzikolo. Jane Chilimampunga ali ndi nkhani yonse

Venancio Mondlane wati anthu alile maliro a Anselmo Vicente ku Mozambique
05:46

AIPAC ku Zambia yatsuta kuwunika ma bilu pomwe paliyamenti itseke pa 15 May 2026
10:17

Anthu 7 aphedwa ku Malawi pogawaganizila kuti akusowetsa maliseche
05:25