Nduna yowona za ntchito mdziko la Malawi olemekezeka a Peter Dimba, ati unduna wawo upitilira kuyendela ma makampani osiyana siyana mdzikolo pofuna kuwonesetsa kuti ma ufulu a ogwila ntchito azilemekezedwa ndi kutetezedwa pamene mayiko pa dziko lonse la pansi akukumbukila anthu ogwila ntchito. Thamo Kapisa wabwela ndi nkhaniyi.

Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
08:07

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
06:12

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11