Zigao zonse khumi za dziko la Zambia lero zachita chisangalalo cha achinyamata cha Youth Day ndipo chapmutu cha chaka chino chili motere: Dzukani ndi Kuuluka . Koma chisangalalo chachikulu cha dziko lonse chayendetsedwa ndi President Hakainde Hichilema mu boma la Solwezi ku chigao cha North-western Province. Daniel Elisha Banda ali ndi nkhani yonse

Mchitidwe wa uchifwamba ukuchulukila ku Malawi
06:53

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wati amayi ndi ofunikila kwambiri
09:57

Mpungwe pungwe wabuka mchipani chotsutsa boma ku Malawi cha MCP
06:45