Zigao zonse khumi za dziko la Zambia lero zachita chisangalalo cha achinyamata cha Youth Day ndipo chapmutu cha chaka chino chili motere: Dzukani ndi Kuuluka . Koma chisangalalo chachikulu cha dziko lonse chayendetsedwa ndi President Hakainde Hichilema mu boma la Solwezi ku chigao cha North-western Province. Daniel Elisha Banda ali ndi nkhani yonse

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

A katswili andale ena ku Malawi ati a Chakwera sanalankhule bwino pa maliro
06:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50