Maboma a Sinda ndi Petauke ku chigao chakum’mawa cha dziko la Zambia apezeka ndi migodi ya mwala wa phosphate. Mwalawu umagwiritsidwa ntchito kupanga feteleza ndipo Gulu la makampani la Wonderful Group of Companies lidzasonkhanitsa ndalama zoposa 2.5 billion US dollars pakukopa makampani akunja kwa dziko kuti adzathandize kukumba mwalawu. Daniel Elisha Banda ali ndi nkhaniyi.

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11

Mchitidwe wa uchifwamba ukuchulukila ku Malawi
06:53

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wati amayi ndi ofunikila kwambiri
09:57