Msonkhano wa mmaiko woimilira chigawo chakum’mwera kwa Africa pa nkhani
ya Ulimi mu Africa womwe umatchedwa KADIPI, wangotha kumene mdziko la Zambia. Mtola nkhani wathu Sydney Katunga Phiri anali nawo ku msonkhanowu ndipo watitumizira ripotili.

Mary Chilima wayamikila Mutharika mtsogoleri wa Malawi pofufuza imfa ya Chilima
08:31

Kachilombo ka Polio 2 kapezeka mu mzinda wa Lusaka ku Zambia
05:48

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wachotsa nduna ziwiri
08:43