Komiti yapadela ya nyumba ya malamulo ku Malawi yomwe inakhazikitsidwa ndi cholinga chofufuza za ngozi yomwe inapha yemwe anali wachiwiri kwa president Dr Saulosi Chilima ndi anthu ena asanu ndi atuta yayamba kupanga wa ngoziyi. George Mhango wabwela ndi nkhani yonse

Chipani cha UPND ku Zambia chachotsa mamembala ake 15
07:02

Chiwonetselo cha za malonda cha International Trade Fair chikuchitika ku Malawi
06:23

Venancio Mondlane wati anthu alile maliro a Anselmo Vicente ku Mozambique
05:46