Mpungwepungwe wabuka mchipani chotsutsa boma cha Malawi Congress Party--MCP mdziko la Malawi pomwe kagulu kena kakufuna mtsogoleri wa Chipanichi Dr Lazarus Chakwera kuti atule pansi udindo wawo pomwe ena akuti kaguluko kangotumidwa chabe. Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.

Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
08:07

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
06:12

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11