Pambuyo pakubedwa kwa mwini wa crossroads hotel ku Lilongwe mdziko la Malawi, tsopano anthu ayamba kumasowa, ena kubedwa kumene, pomwenso ena akumapezeka ataphedwa patapita masiku. Ena akumawaba nkukawagwi-li-li-ra atawamwetsa mankhwala ogonetsa. Jayne Chilimampunga wabwela ndi nkhani yonse.

Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
08:07

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
06:12

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11