Boma la dziko la Zambia liri ndi nkhawa ndi mchitidwe wa anthu otengela lamulo m’manja mwawo pamene munthu wapalamula ndipo polisi yati izathana ndi aliyense ochita zimenezi. Ziyenela Zimba wabwela ndi nkhani yonse

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

A katswili andale ena ku Malawi ati a Chakwera sanalankhule bwino pa maliro
06:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50