Boma la Zimbabwe lalengeza kuti kugulitsa miyala ya mtengo wa patali kuyimitsidwe kufikila mtsogolo chifukwa chokuti miyala imagulitsidwa osasulidwa zomwe zimapangitsa kuti miyala izigulitsidwa motsika mtengo. John Kassim akulongosola

Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
08:07

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
06:12

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11