Raphael Tuju, yemwe ndi Nduna yakale yoona za ubale pakati pa dziko la Kenya ndi mayiko ena , amupeza ndipo amumanga kamba konamilizira kuti wasowa komanso kuti anabedwa.Mkulu wotsogolera kafukufuku ku polisi ya Nairobi a Mohamed Amin, anena pa msonkhano wa atolankhani kuti a Tuju anali mkati mwa nyumba yake nthawi yonseyi, ndipo anafotokoza kuti kusowa kwa Tuju kunali kokonzedwa mwadala osati kubedwa ndi anthu achipongwe. Mtolankhani mzathu ku m'mawa kwa Africa Alfred Dzaoneni ali ndi zambiri.

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

A katswili andale ena ku Malawi ati a Chakwera sanalankhule bwino pa maliro
06:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50