Kusowa kwa ena mwa mapepala(Documents) mu ripoti lokhudza kumangidwa kwa nkulu wa bungwe lothana ndi ziphuphu ndi katangale mdziko la Malawi mai Martha Chizuma, kwadzutsa Mapiri pachigwa.
A Malawi ambiri pamodzi ndi mabungwe ena sakukondwa ndi zomwe zatulutsidwazi .Mntsogoleri wa dzikoli Rev. Dr. Lazarus McCarthy Chakwera, adakhazikitsa gulu la anthu khumi ndi mmodzi(11) kuti afufuze za kumangidwa kwa mai Chizuma, yemwe patsikulo ankayenera kukaonana ndi mntsogoleri wadzikolo.

Nyumba ya malamulo ku Malawi yakhazikitsa komiti yofufuza imfa ya a Chilima
08:07

Mtsogoleri wachipani chotsutsa cha NUP ku Uganda Bobi Wine watuluka mdzikolo
06:12

Achinyamata ku Zambia ati achinyamata apatsidwe mwayi otukula miyoyo yawo
09:11