Anthu pafupifupi 300 amene akukhudzidwa ndi kuphedwa mwa nkhanza kwa mai wa ntchito za malonda, Hellen Kamutumbe , amangidwa ndi A polisi mu boma la Kalumbila ku chigao cha North-western Province cha dziko la Zambia. Maiyu anavulidwa ndi kugendedwa miyala ndi anthu okwiya Lachisanu lathali pamene mnyamata wa zaka 25 zakubadwa ananamizila maiyu kuti anamubela maliseche ake mwa matsenga pa msika wa Kisasa mu bomali. Daniel Elisha Banda akulongosola.

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

A katswili andale ena ku Malawi ati a Chakwera sanalankhule bwino pa maliro
06:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50