Alimi ambiri mdziko la Zambia, akudandaula kuti boma likuchedwa kuwapatsa ndalama zawo pa zokolola zawo zomwe anagulitsa ku bungwe la boma lowona za chakudya la Food Reserve agency chaka chatha pamene boma linalonjeza kuti liwalipira alimi onse a mdzikolo pofika pa 10 January chaka chino. Ziyenela Zimba wabwela ndi nkhani yons

Anthu a chi alubino akupitilira kuchitidwa nkhanza ku Malawi
07:17

Akatswili a ndale ati A Mutharika akutsogolera bwino Malawi
06:24

MICHAEL CHANG AKUFUNA KUTI ATULUTSIDWE MNDENDE KU AMERICA
08:31