Mtsogoleri wa dziko la Zambia Hakainde Hichilema wachotsa ntchito atsogoleri omwe anali mu bungwe lomwe limayang'anira chigao cha Anti-Corruption Commission chomwe chimalimbana ndi ziphupu komanso katangale mdzikolo . Mkulu wa bungwe la achinyamata la Youth Development Foundation, Muyeye Chinoya , wati chiganizo cha President Hichilema pa nkhaniyi chilibwino. Daniel Elisha Banda ali wadza ndi nkhani yonse.