Mankhwala aboma la Zambia pa muyeso wa 65 million US dollars apezeka ku nkhokwe yosunga katundu yomwe ili mmanja mwa anthu wamba ,Mwa ichi, President Hakainde Hichilema wachotsa nduna ya za umoyo ,Sylvia Masebo, ndikuipereka ku unduna wa za nthaka.
Anthu wamba ndi akuluakulu ena azipani zotsutsa adzudzula ganizo la President Hichilema.
Daniel Elisha Banda wadza ndi nkhani yonse.