Anthu a mdziko la Malawi ati dzikolo silikutukuka mu zinthu zambiri ngakhale likukondwelera kuti lakwanitsa zaka 62 chikhalireni pa ufulu odzilamulira kuyambila mchaka cha 1964. Jayne Chilamampunga wamva maganizo katswili olankhula pa nkhani zosiyana siyana mdzikolo a Imran Saidi

Msonkhano wa zi ntchito za njanji wa Africa Rail wamalizika
06:14

Mabungwe ena ku Zambia ati a Hichilema asapange kampeni ndi katundu wa boma
08:44

Chionetselo cha za malonda cha Internationational Trade Fair chatha ku Zambia
06:54