Chipani cha United Transformation Movement -UTM cha mdziko la Malawi chalengeza kuti tsopano chatuluka mumgwirizano omwe chinapanga ndi chipani cha Malawi Congress Party -MCP otchedwa Tonse Alliance. izitu zanenedwa pamsonkhano wa atolankhani lero mumzinda wa Lilongwe. Mtolankhani mzathu Kondwani Nyamasauka anali nawo pa msonkhanowu ndipo akusimba