Banki yaikulu ya mdziko la Zambia ya Bank of Zambia ikukonza chiganizo chakuyimitsa kugwiritsa ntchito ndalama zaku maiko akunja mu ntchito zamalonda zomwe zimachitika mkati mwa dzikolo.
Bankiyi ili ndi maganizo akuti chiletso chimenechi chidzalimbitsa mphamvu za ndalama ya kwacha komanso maziko azachuma cha dzikolo.
Koma mkulu wa Tour Guides Association wa nkhalango yaku South Luangwa National Park m’boma la Mambwe, Suzyo Zimba ,wati chiganizo chimenechi chidzapha ma business ambiri.
Nkhani yonse ili ndi Daniel Elisha Banda.