Zomwe anayankhula mtsogoleri wakale wa dziko la Malawi Dr Lazarus Chakwera kuti anthu asamutengere ku mtoso ndi munthu okonda mtendere zautsa zoyankhula zosiyana pakati pa Malawi. Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.

Mabungwe ena ku Malawi adzudzula zomwe Alexious Kamangila akulankhula
07:45

Mtsogoleri wa South Sudan Salva Kiir wachotsa sipikala wa nyumba ya Malamulo
05:50

Mchitidwe wa anthu otengela lamulo m’manja wakula ku Zambia
06:26