M’modzi mwa akatswiri a za umoyo pa matenda opatsira pogonana mu dziko la Malawi, George Jobe walankhula pa kufunika kuphunzitsa anthu pa chiopyezo kwa kugonana kosadziteteza. Mtolankhani wathu Hastings Blessings Jumbe akusimba.

MUUNI WA ZA LUSO LA MAKONO NDI DANIEL BANDA
08:53

BUNGWE LA UNITED PURPOSE KU MOZAMBIQUE LIKHAZIKITSA MALO OTUNGIRA MADZI A UKHONDO
05:56

NJOBVU ZAYAMBA KUSAMUTSIDWA KUCHOKA KU LIWONDE NATIONAL PARK KU MALAWI
04:49