Bungwe la United Purpose mu dziko la Mozambique, likufuna kukhazikitsa ntchito yopereka madzi a ukhondo ochokera mu mpope m’ma midzi. Bungweli, lati projectiyi ndi ya ndalama zokwana $10milion, ndipo alimi athandizika pa nkhani yosowa madzi. Mtolankhani wathu Bright Sonjera wadza ndi nkhaniyi.

MUUNI WA ZA LUSO LA MAKONO NDI DANIEL BANDA
08:53

NJOBVU ZAYAMBA KUSAMUTSIDWA KUCHOKA KU LIWONDE NATIONAL PARK KU MALAWI
04:49

ANTHU ASANU AGAMULIDWA KUTI AKHALE MDENDE MOYO WAWO ONSE KU MALAWI
06:11