News in ChinyanjaNews in Chinyanja

ANTHU ASANU AGAMULIDWA KUTI AKHALE MDENDE MOYO WAWO ONSE KU MALAWI

View descriptionShare

Anthu ambiri alankhulapo pa gamulo lomwe bwalo la milandu mdziko la Malawi, lagamula kuti anthu asanu omwe anapha mwa nkhanza munthu wa chi albino, Mc Donald Masambuka mu chaka cha 2018 akhale m’nende moyo wawo onse. Mtolankhani wathu Jane Chilimampunga wadza ndi nkhaniyi.    

  • Facebook
  • Twitter
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

News in Chinyanja

A news and current affairs show produced live by the current affairs team.
Social links
Recent clips
Browse 2,102 clip(s)