Anthu ambiri alankhulapo pa gamulo lomwe bwalo la milandu mdziko la Malawi, lagamula kuti anthu asanu omwe anapha mwa nkhanza munthu wa chi albino, Mc Donald Masambuka mu chaka cha 2018 akhale m’nende moyo wawo onse. Mtolankhani wathu Jane Chilimampunga wadza ndi nkhaniyi.

MUUNI WA ZA LUSO LA MAKONO NDI DANIEL BANDA
08:53

BUNGWE LA UNITED PURPOSE KU MOZAMBIQUE LIKHAZIKITSA MALO OTUNGIRA MADZI A UKHONDO
05:56

NJOBVU ZAYAMBA KUSAMUTSIDWA KUCHOKA KU LIWONDE NATIONAL PARK KU MALAWI
04:49