News in ChinyanjaNews in Chinyanja

NJOBVU ZAYAMBA KUSAMUTSIDWA KUCHOKA KU LIWONDE NATIONAL PARK KU MALAWI

View descriptionShare

Boma la Malawi layamba ntchito yosamutsa njobvu zokwana 250 komanso nyama zina ndi zina kuchokera ku Liwonde National Park kupita ku Kasungu National Park, komwe ndi malire ndi dziko la Zambia.  

Mtolankhani wathu George Mhango walankhula ndi Bright Kumchedwa yemwe mkulu wa bungwe loyang’anira malo osungira nyama zakutchire pa ntchitoyi.   

  • Facebook
  • Twitter
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

News in Chinyanja

A news and current affairs show produced live by the current affairs team.
Social links
Recent clips
Browse 2,102 clip(s)