News in ChinyanjaNews in Chinyanja

NTCHITO ZOKOPA ALENDO KU MALAWI ZAKHUZIDWA KWAMBILI NDI MLILI WA COVID-19

View descriptionShare

CHINYANJA: Nduna ya zokopa alendo ku dziko la Malawi Micheal Usi wati ntchito zokopa alendo mdzikolo zapita pansi kwambili chifukwa cha kubuka kwa mlili wa covid-19, dziko la Malawi linakhazikitsa mwezi wa September kuti ndi mwezi wantchito zokopa alendo.

 

ENGLISH: Malawi’s tourism minister Micheal Usi has said that tourism activities have been adversely affected by the Covid-19 pandemic. Malawi observes the month of September as tourism month.

  • Facebook
  • X (Twitter)
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

News in Chinyanja

A news and current affairs show produced live by the current affairs team.
Social links
Recent clips
Browse 2,102 clip(s)