News in ChinyanjaNews in Chinyanja

NKULU WA BUNGWE LA BUTEZ KU ZAMBIA WATI BOMA LILEMBE NTCHITO NZIKA ZA ZAKA 45

View descriptionShare

Nkulu wa bungwe la aziphunzitsi la Basic Education Teachers Union of Zambia kuchigawo cha kummawa Simon Botha wati chingakhale chinthu chobweretsa nsangala ngati boma lingalembe ntchito aphunzitsi a zaka zokwana 45 zakubadwa kapena kupyola pangono, Malamulo a dziko la Zambia amaletsa boma kulemba anthu a zaka zimenezi ntchito. Daniel Elisha Banda, Zambia.

  • Facebook
  • Twitter
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

News in Chinyanja

A news and current affairs show produced live by the current affairs team.
Social links
Recent clips
Browse 2,102 clip(s)