News in ChinyanjaNews in Chinyanja

MTSOGOLERI WA DZIKO LA ZAMBIA WATI MAFUMU AKUYENERA KUKWEZA NAWO CHITUKUKO

View descriptionShare

Anthu mu dziko la Zambia apelenga ndemanga pa mawu omwe mtsogoleri wadzikolo Hakainde Hichilema, walankhula kuti nzika za dzikolo komanso mafumu, atenge nawo gawo pa mbali yokweza chitukuko cha dzikolo. Mtolankhani wathu Ziyenela Zimba walankhula ndi Headman Kalinde wa m’chigawo cha ku m’mawa kwa dzikolo pa nkhaniyi.  

  • Facebook
  • Twitter
  • WhatsApp
  • Email
  • Download

News in Chinyanja

A news and current affairs show produced live by the current affairs team.
Social links
Recent clips
Browse 2,102 clip(s)