CHINYANJA: Amene anali ndi mkulu wa polisi mdziko la Malawi a George Kainja atulutsidwa pa belo lero pambuyo pomangidwa dzulo pa mlandu olowelela pa kafuku fuku wa katangale yemwe mpondamatiki Zuneth Sattar anachita.

MUUNI WA ZA LUSO LA MAKONO NDI DANIEL BANDA
08:53

BUNGWE LA UNITED PURPOSE KU MOZAMBIQUE LIKHAZIKITSA MALO OTUNGIRA MADZI A UKHONDO
05:56

NJOBVU ZAYAMBA KUSAMUTSIDWA KUCHOKA KU LIWONDE NATIONAL PARK KU MALAWI
04:49