Boma la Zimbabwe lakana nkhani yokuti chakudya chikupelewela kwa anthu amene ali ku Bulawayo omwe achoka ku South Africa pambuyo powukilidwa chifukwa chokhala mdzikolo mosavomelezeka . John Kassim akusimba...

Bungwe la MANEB ku Malawi latulutsa zotsatila za mayeso a standadi 8 ndi fomu 2
05:42

Polisi ya Zambia yagwira akuluakulu 11 azipani zotsutsa za mgwirizano wa Tonse
09:16

Mabungwe ku Zimbabwe adzudzula boma kuti likuwononga ufulu opanga zionetselo
05:06