Mabungwe omenyela ufulu anthu mdziko la Zimbabwe, adandaula kuti boma likuphwanya ma ufulu a anthu pamene anthu ena anamangidwa lachisanu sabata yatha chifukwa chofuna kuchita zionetselo. John Kassim akulongosola zonse..

Bungwe la MANEB ku Malawi latulutsa zotsatila za mayeso a standadi 8 ndi fomu 2
05:42

Polisi ya Zambia yagwira akuluakulu 11 azipani zotsutsa za mgwirizano wa Tonse
09:16

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wadzudzula ziwawa pa ndale
05:09