Polisi ya dziko la Zambia yagwira akuluakulu khumi ndi m’modzi 11 azipani zotsutsa za mgwirizano wa Tonse Alliance pambuyo pakupezeka ndi zida za nkhondo zoopsya. Mkulu wa zipanizi ndi a Brian Mundubile amene akutengako mbali ku masankho a President.
Pakati pa wogwidwawa pali mpongozi wa malemu Edgar Chagwa Lungu, a Patrick Mwansa. Mlembi wa cabinet ya boma.
A Patrick Kangwa ndi amene alengeza nkhaniyi ku mtundu wa Zambia. Daniel Elisha Banda ali ndi nkhani yonse.

Bungwe la MANEB ku Malawi latulutsa zotsatila za mayeso a standadi 8 ndi fomu 2
05:42

Mabungwe ku Zimbabwe adzudzula boma kuti likuwononga ufulu opanga zionetselo
05:06

Mtsogoleri wa Zambia Hakainde Hichilema wadzudzula ziwawa pa ndale
05:09