Oyimba wa Ku Malawi Mr Thompo walimbikitsa oyimba a mdziko la South Africa amene anachoka ku mudzi ku Malawi ndipo tsopano akuyimba mdzikoli pamene walankhula ndi Stella Longwe pa pologalamu ya Malonje.
Malonje (Chinyanja)
18 clip(s)
Ndakatulo yolira a Saulos Chilima ndi anthu ena asanu ndi atatu ku Malawi
Oyimba wa ku Malawi Master Manda waonetsa kuti khama limapindula
Malonje