President wa dziko la Malawi Dr Lazarus Chakwera,anatsogolera a Malawi pa mwambo okumbukila malemu Saulos Chilima yemwe anali wachiwiri wawo ndipo mwambowu unachitikira m’boma la Mzimba pamene akubanja nawo anali ndi mwambo ngati omwewu ku kumudzi kwa Chilima m’boma la ntcheu. Mtolankhani mzathu mdziko la Malawi Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.

Oyimba wa mdziko la Mozambique BS Music wati oyimba asamayike maso pa ndalama
13:35

Mada Phiri kucheza ndikatswili oyimba wa mdziko la DRC Feed Paul RP amene amadziwika
13:05

Oyimba wa manganje wa ku Mozambique Ricabana wati amanyadila kuyimba za chimidzi
10:48