Mkulu wa bungwe la CDEDI mdziko la Malawi a Sylvester Namiwa awapatsa milandu iwiri , yofuna kulanda boma mwa upandu ndi kugawa uthenga wabodza. A Namiwa pakali pano akusungidwa ku ndende ya Maula pamene akuyembekezela kuti apatsidwe belo. George Mhango wabwela ndi nkhaniyi

Bungwe la MANEB ku Malawi latulutsa zotsatila za mayeso a standadi 8 ndi fomu 2
05:42

Polisi ya Zambia yagwira akuluakulu 11 azipani zotsutsa za mgwirizano wa Tonse
09:16

Mabungwe ku Zimbabwe adzudzula boma kuti likuwononga ufulu opanga zionetselo
05:06