Pamene ngozi komanso kuonongeka kwa katundu wa mu misewu ikulu ikulu kwafika poonjeza mdziko la Malawi, spikala wa nyumba yamalamulo mdzikolo wapempha aphungu kuti akhazikitse lamulo lokhwimitsa zilango kwa anthu omwe amayendetsa galimoto ataledzera ndi kugwetsa mapolo amagetsi amunsewo azikonza okha zinthuzi.
Kondwani Nyamasauka wadza ndi zambiri mu report ili.

Bungwe la MANEB ku Malawi latulutsa zotsatila za mayeso a standadi 8 ndi fomu 2
05:42

Polisi ya Zambia yagwira akuluakulu 11 azipani zotsutsa za mgwirizano wa Tonse
09:16

Mabungwe ku Zimbabwe adzudzula boma kuti likuwononga ufulu opanga zionetselo
05:06